LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsa. 10
  • Muziyang’ana kwa Yehova Kuti Mupeze Citonthozo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Muziyang’ana kwa Yehova Kuti Mupeze Citonthozo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mukayika-kayika Mpaka Liti?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Citsanzo Cimene Tingatengele pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Kodi Mukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Kodi Mumaugwila Mtima?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 September tsa. 10

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muziyang’ana kwa Yehova Kuti Mupeze Citonthozo

Eliya anacita mantha, ndipo anathaŵa kuti apulumutse moyo wake (1 Maf. 19:3, 4; w19.06 15 ¶5)

Yehova anam’patsa thandizo lofunikila na kumuonetsa mphamvu zake zocititsa mantha (1 Maf. 19:5-7, 11, 12; ia 103 ¶13; 106 ¶21)

Yehova anapatsa Eliya nchito yakuti agwile (1 Maf. 19:15-18; ia 106 ¶22)

M’bale amene ali m’ndende akulalikila msilikali wolondela ndende.

Masiku ano, Yehova amakamba nafe kupitila m’Mawu ake, Baibo. Iye amatikumbutsa kuti amatikonda kwambili, ndipo watipatsa nchito yabwino yoti tizigwila.—1 Akor. 15:58; Akol. 3:23.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani