LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 September tsa. 9
  • Samalani na Nkhani Zabodza

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Samalani na Nkhani Zabodza
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Pewani Kutengela Elifazi Popeleka Citonthozo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • ‘Kodi Munthu Angakhale Waphindu kwa Mulungu?’
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Yehova Amakondwela Tikamapemphelela Ena
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Limbikitsani Ena ndi Mau Abwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 September tsa. 9

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Samalani na Nkhani Zabodza

Zimene Elifazi anakamba zinaoneka ngati zoona cifukwa iye anali wamkulu komanso wanzelu (Yobu 4:1; it-1 713 ¶11)

Posonkhezeledwa na ziwanda, Elifazi anakamba mawu olefula kwa Yobu (Yobu 4:​14-16; w05 9/15 26 ¶2)

Zina zimene iye anakamba zinali zoona, koma anazigwilitsa nchito molakwika (Yobu 4:19; w10 2/15 19 ¶5-6)

M’bale akuyang’ana pa foni yake.

Dziko la Satanali lapitiliza kufalitsa nkhani zabodza komanso zowononga.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimayamba nafufuza kuti nitsimikize ngati nkhani imene namva ni yoona?’—mrt-CN 32 ¶13-17.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani