LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 9
  • Makolo—Phunzitsani Ana Anu Kukondweletsa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Makolo—Phunzitsani Ana Anu Kukondweletsa Mulungu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Zisankho Zimene Zimaonetsa Kuti Timadalila Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Seŵenzetsani Mfundo za m’Baibo Pothandiza Ana Anu Kuti Apambane
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Kufuna-funa Nzelu mwa Kuŵelenga Baibo Tsiku Lililonse
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Zimene Tiphunzilapo pa Mawu Othela Omwe Amuna Okhulupilika Anakamba
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 9
Zithunzi: Zida zophunzitsila acicepele. 1. Ana a misinkhu yosiyanasiyana ali na buku lakuti “Phunzirani Kwa Mphunzitsi Waluso.” 2. Buku la “Phunzirani Kwa Mphunzitsi Waluso.” 3. Kamtsikana kacicepele kali na buku lake lakuti “Buku Langa la Nkhani za M’baibo.” 4. Kamtsikana kenanso kakuŵelenga buku lakuti “Buku Langa la Nkhani za M’baibo.” 5. Mtsikana akuŵelenga buku lakuti “Your Youth​—Getting the Best out of It” pa msonkhano wacigawo. 6. Kam’nyamata kakupenta zithunzi pa zocita za ana zopezeka pa jw.org. 7. Cithunzi ca m’bulosha yakuti “Zimene Ndimaphunzila m’Baibo.” 8. Cithunzi coonetsa Kalebe na Sofiya a m’mavidiyo yakuti “Khala Bwenzi la Yehova.” 9. Buku lakuti “Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo.” Cithunzi ca m’buku cionetsa Samisoni akukankha zipupa ziŵili na mphamvu zake zonse.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Makolo—Phunzitsani Ana Anu Kukondweletsa Mulungu

Yehova amaona kuti acicepele ni amtengo wapatali. Iye amaona mmene amapitila patsoglo mwauzimu komanso zimene amapilila. (1 Sam. 2:26; Luka 2:52) Ngakhale atakhala kuti ni acicepele kwambili, ana angakondweletse mtima wa Yehova mwa khalidwe lawo labwino. (Miy. 27:11) Mwa gulu lake, Yehova wapeleka zida zabwino kwambili zothandiza makolo kuphunzitsa ana awo kuti azikonda Yehova na kumumvela.

TAMBANI VIDIYO YAKUTI ACICEPELE—YEHOVA AMAKONDWELA MUKAMAPILILA! KENAKO YANKHANI MAFUNSO AYA:

  • Kwa zaka, kodi Yehova wakhala akupeleka malangizo otani othandiza acicepele?

  • Kodi pali zida zotani zothandiza makolo kuphunzitsa ana?

  • Ngati ndinu wacicepele, kodi Yehova wakupatsani ciyani cimene cakupindulilani? Nanga mwapindula motani?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani