LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 13
  • Zimene Ningacite Kuti Niteteze Mbili Yabwino ya Gulu Lathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Ningacite Kuti Niteteze Mbili Yabwino ya Gulu Lathu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Zisankho Zimene Zimaonetsa Kuti Timadalila Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Lembani Mmene Mwapitila Patsogolo
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Kufuna-funa Nzelu mwa Kuŵelenga Baibo Tsiku Lililonse
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Muzivomeleza Kuti Pali Zimene Simudziwa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2025
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 13

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Zimene Ningacite Kuti Niteteze Mbili Yabwino ya Gulu Lathu

Anthu amaona khalidwe la Mboni za Yehova. (1 Akor. 4:9) Tingadzifunse kuti, ‘Kodi zokamba na zocita zanga zimapeleka ulemelelo kwa Yehova?’ (1 Pet. 2:12) Mosakayikila, sitifuna kucita ciliconse cimene cingawononge mbili yabwino imene Mboni za Yehova zakhala nayo kwa zaka zambili.—Mlal. 10:1.

Pa zocitika zotsatilazi, lembani zimene Mkhristu ayenela kucita komanso mfundo yothandiza ya m’Baibo:

  • Munthu amene si Mboni wakunyozani mwaukali

  • Zovala zanu, motoka, kapena nyumba yanu n’zakuda

  • Lamulo la boma silinakukomeleni kapena n’lovuta kulitsatila

Zithunzi: Tumapikica twa muvidiyo yakuti “Timakonda na Kulemekeza Coonadi.” 1. M’bale akuŵelenga m’buku lofufuzila. 2. M’bale na mlongo akuona malifalensi a mabuku ofufuzila. 3. Mapepala a nkhani zofufuzidwa pafupi na bulosha lakuti “Mmene Moyo Unayambira​—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri.” 4. Mlongo akuyang’ana pa webusaiti ya jw.org pa foni yake.

Kodi ofufuza a m’Dipatimenti Yolemba Mabuku amacita ciyani kuti tikhalebe na mbili yabwino?

TAMBANI VIDIYO YAKUTI TIMAKONDA NA KULEMEKEZA COONADI, KENAKO YANKHANI FUNSO ILI:

N’ciyani cakukondweletsani poona zimene gulu lathu limacita kuti likonze nkhani zolondola?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani