LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 142
  • Tigwilitsitse Ciyembekezo Cathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tigwilitsitse Ciyembekezo Cathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 142

NYIMBO 142

Tigwilitsitse Ciyembekezo Cathu

Yopulinta

(Aheberi 6:18, 19)

  1. 1. Zaka zambili-mbili anthu pa dziko

    Adzandiladi mosaphula kanthu.

    Mwacisoni ali mu ukapolo

    Cifukwa onse ni ocimwa.

    (KOLASI)

    Ufumu wa Mulungu wafika!

    Khristu adzatimasula ku mantha.

    Posacedwa zoipa zidzatha.

    Ciyembekezoci citilimbitsa.

  2. 2. Tsiku la Yehova M’lungu layandika!

    Anthu sadzalilanso: “Mpaka liti?”

    Yehova ‘dzamasula cilengedwe.

    Tim’tamande ndipo tiimbe.

    (KOLASI)

    Ufumu wa Mulungu wafika!

    Khristu adzatimasula ku mantha.

    Posacedwa zoipa zidzatha.

    Ciyembekezoci citilimbitsa.

(Onaninso Sal. 27:14; Mla. 1:14; Yow. 2:1; Hab. 1:2, 3; Aroma 8:22.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani