LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 24
  • Bwelani ku Phili la Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bwelani ku Phili la Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Bwerani Kuphiri la Yehova
    Imbirani Yehova
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tilalikile kwa Anthu a Makhalidwe Onse
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 24

NYIMBO 24

Bwelani ku Phili la Yehova

Yopulinta

(Yesaya 2:2-4)

  1. 1. Taonani phili,

    Lokwezeka la M’lungu,

    Ilo ni phili la

    kulambila koona.

    Anthu ocokela,

    ku malo akutali.

    Abwela alambile

    Atate Yehova.

    Tsopano ocepa

    Akhala mtundu waukulu,

    Cifukwa Yehova

    amadalitsa nchito yathu.

    Anthu oculuka

    abwela kwa Yehova,

    Kuti acilikize

    Ucifumu wake.

  2. 2. Yesu, Mfumu yathu,

    Analamula kuti

    Ise tilalikile,

    uthenga wabwino.

    Iye aitana anthu,

    onse omvela.

    Kuti aphunzitsidwe

    mau a Yehova.

    Khamu lalikulu,

    onani mmene lakulila.

    Ndise okondwela

    kuti tili mu gulu ili.

    Tiyeni tiimbe,

    tiitanile ena

    Kuti nawo abwele,

    Ku phili la M’lungu.

(Onaninso Sal. 43:3; 99:9; Yes. 60:22; Mac. 16:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani