LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 69
  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
  • Patsogolo! Inu Mboni Zake
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 69

NYIMBO 69

Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!

Yopulinta

(2 Timoteyo 4:5)

  1. 1. Pitani, kalalikileni

    Kwa amitundu yonse.

    Na mtima wokonda anansi,

    Thandizani ofatsa.

    Ni mwayi wathu kulengeza

    Za Ufumu wa Yehova.

    Mokondwa tiphunzitsa ena,

    Za dzina lake loyela.

    (KOLASI)

    Lalikani uthenga wa Ufumu

    konse konse.

    Khalanibe okhulupilika

    kwa M’lungu wathu.

  2. 2. Capamodzi titumikile

    Yehova, ‘tate wathu.

    Odzozedwa na nkhosa zina,

    Tiphunzitse co’nadi.

    Onse tiŵauze uthenga,

    Wa Ufumu wa Yehova.

    Tilengeza molimba mtima

    Timadalila Yehova.

    (KOLASI)

    Lalikani uthenga wa Ufumu

    konse konse.

    Khalanibe okhulupilika

    kwa M’lungu wathu.

(Onaninso Sal. 23:4; Mac. 4:29, 31; 1 Pet. 2:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani