LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 61
  • Patsogolo! Inu Mboni Zake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Patsogolo! Inu Mboni Zake
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Patsogolo na Ulaliki wa Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 61

NYIMBO 61

Patsogolo! Inu Mboni Zake

Yopulinta

(Luka 16:16)

  1. 1. Mboni za Yehova n’zolimba mtima

    Zimalengeza Ufumu wa Yehova.

    Ngakhale Satana ‘zizunze,

    Sizileka, zidalila Yehova.

    (KOLASI)

    Imwe Mboni za M’lungu, limbani mtima!

    Tumikilani Yehova na cimwemwe!

    Uzani onse kuti omvela M’lungu

    Adzakhala m’dziko latsopano.

  2. 2. Atumiki a Yehova Mulungu,

    Sacita mantha polalikila anthu.

    Samakonda zinthu za m’dziko;

    Iwo saiŵala Mulungu wao.

    (KOLASI)

    Imwe Mboni za M’lungu, limbani mtima!

    Tumikilani Yehova na cimwemwe!

    Uzani onse kuti omvela M’lungu

    Adzakhala m’dziko latsopano.

  3. 3. Anthu amanyoza dzina la M’lungu.

    Samalemekeza ucifumu wake.

    Tiyeni’se tiwacenjeze;

    Tidziŵikitse dzina la Yehova.

    (KOLASI)

    Imwe Mboni za M’lungu, limbani mtima!

    Tumikilani Yehova na cimwemwe!

    Uzani onse kuti omvela M’lungu

    Adzakhala m’dziko latsopano.

(Onaninso Eks. 9:16; Afi. 1:7; 2 Ti. 2:3, 4; Yak. 1:27.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani