LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 32
  • Ima ku Mbali ya Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ima ku Mbali ya Yehova
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani ku Mbali ya Yehova
    Imbirani Yehova
  • Ndimakondwera Kucita Cifuniro Canu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 32

NYIMBO 32

Ima ku Mbali ya Yehova

Yopulinta

(Ekisodo 32:26)

  1. 1. Panthawi ina ise tinali

    Mbali ya cipembedzo conama.

    Komabe, tinasangalaladi

    Kumvela za Ufumu.

    (KOLASI)

    Sankhani Yehova; mumtumikile.

    Sadzakusiyani; mvelani iye

    Ndipo lengezani Ufumu wake.

    Muŵauze onse Khristu ni Mfumu.

  2. 2. Tigwilizane, tilalikile

    Uthenga wabwino wa Ufumu.

    Nthawi yafika anthu asankhe

    Kutumikila M’lungu.

    (KOLASI)

    Sankhani Yehova; mumtumikile.

    Sadzakusiyani; mvelani iye

    Ndipo lengezani Ufumu wake.

    Muŵauze onse Khristu ni Mfumu.

  3. 3. Ise sitimayopa Satana,

    Timadalila Mulungu wathu.

    Ngakhale adani aculuke,

    M’lungu ni mphamvu yathu.

    (KOLASI)

    Sankhani Yehova; mumtumikile.

    Sadzakusiyani; mvelani iye

    Ndipo lengezani Ufumu wake.

    Muŵauze onse Khristu ni Mfumu.

(Onaninso Sal. 94:14; Miy. 3:5, 6; Aheb. 13:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani