LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 8
  • Mgonero wa Ambuye

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mgonero wa Ambuye
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mgonelo wa Ambuye
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova
  • Lomba Ndise Thupi Limodzi
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 8

Nyimbo 8

Mgonero wa Ambuye

(Mateyo 26:26-30)

1. Atate wathu wakumwamba,

Usikuwu n’ngwapadera!

Pa Nisani fotini panaoneka

Chikondi, nzeru ndi mphamvu.

Mwanawankhosa anadyedwa,

Is’raeli namasuka.

Kenako Mbuye anakhetsa magazi

Kukwaniritsa ulosiwo.

2. Tasonkhana pamaso panu.

Tadza ngati nkhosa zanu

Kukutamandani pa chikondi chanu,

Dzina lanu tilikweze.

Tisunge Chikumbutso ichi,

m’mitima ndi m’maganizo.

Tidzamutsatira Khristu nthawi zonse

Kuti tidzaupeze moyo.

(Onanino Luka 22:14-20; 1 Akor. 11:23-26.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani