LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 36
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 36

Nyimbo 36

“Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

(Mateyo 19:5, 6)

1. Mulungu ndi anthu

Amva malonjezo.

Chingwe cholimba bwino

Chamangidwa lero.

Awa alonjezana

Kuti akondane.

(KOLASI)

‘Chomwe M’lungu wamanga

Musalekanitse.’

2. Cholinga cha M’lungu

Anachifufuza.

Kupeza madalitso

N’komwe akufuna.

Awa agwirizana

Kuti akondane.

(KOLASI)

‘Chomwe M’lungu wamanga

Musalekanitse.’

(Onaninso Gen. 2:24; Mla. 4:12; Aef. 5:22-33.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani