LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 87
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Lomba Ndise Thupi Limodzi
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 87

Nyimbo 87

Tsopano Ndife Thupi Limodzi

(Genesis 2:23, 24)

1. Fupa la mafupa anga,

Ndiwe mnofu wa mnofu wanga.

M’lungu wandipatsa mnzanga,

Inde wangawanga.

Tsopano tili amodzi,

Yehova ankafuna chonchi.

Monga mwamuna ndi mkazi,

Banja n’limeneli.

Mulungu atitsogolera.

Tsiku ndi tsiku

Chikondi tisonyeza.

Mmene talonjezerana

Zichitike, tizikondana.

Tilemekeze Yehova,

Ndipo ukhalebe wanga.

(Onaninso Gen. 29:18; Mlal. 4:9, 10; 1 Akor. 13:8.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani