LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 129
  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tigwilitsitse Ciyembekezo Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 129

Nyimbo 129

Tigwire Mwamphamvu Chiyembekezo Chathu

(Aheberi 6:18, 19)

1. Anthu akhala akuyenda mumdima

Ndipo sanapindule kanthu n’komwe.

Zadziwika kuti anthu ochimwa

Kuvutika sangakuchotse.

(KOLASI)

Tiyeni tiimbe mokondwera

Poti Ufumu wa M’lungu wafika!

Yesu adzachotsadi zoipa,

Chiyembekezochi n’chonga nangula.

2. Uthenga womwe ukumveka ndi woti:

“Tsiku la Mulungu layandikira.”

Anthu ake sadzamvanso chisoni

M’lungu wathu timuimbira.

(KOLASI)

Tiyeni tiimbe mokondwera

Poti Ufumu wa M’lungu wafika!

Yesu adzachotsadi zoipa,

Chiyembekezochi n’chonga nangula.

(Onaninso Hab. 1:2, 3; Sal. 27:14; Yow. 2:1; Aroma 8:22.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani