LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 64
  • Timasangalala Kuthandizila pa Nchito Yokolola

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Timasangalala Kuthandizila pa Nchito Yokolola
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tigwire Ntchito Yokolola Mosangalala
    Imbirani Yehova
  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • Tikhala Monga mwa Dzina Lathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 64

NYIMBO 64

Timasangalala Kuthandizila pa Nchito Yokolola

Yopulinta

(Mateyu 13:1-23)

  1. 1. Ino ni nthawi yokolola,

    Ni mwayi wosangalatsa.

    Onani mindayo yayela,

    Tiyeni ticite cangu.

    Yesu amatitsogolela,

    Pamene tilalikila.

    Timayamikila nchito iyi,

    Timaicita mokondwa.

  2. 2. Tigwile nchitoyi mwakhama,

    Pokonda anthu na M’lungu.

    Tiphunzitse onse mwam’sanga,

    Mapeto ayandikila.

    Cimwemwe cimene tipeza,

    N’dalitsodi la Yehova.

    Tigwile nchitoyi mosaleka,

    M’lungu adzatidalitsa.

(Onaninso Mat. 24:13; 1 Akor. 3:9; 2 Tim. 4:2.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani