LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 118
  • “Tiwonjezeleni Cikhulupililo”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Tiwonjezeleni Cikhulupililo”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Imbirani Yehova
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 118

NYIMBO 118

“Tiwonjezeleni Cikhulupililo”

Yopulinta

(Luka 17:5)

  1. 1. O Yehova, ise ndise ocimwa,

    Mtima wathu ‘mafuna zoipa.

    Nthawi zina ise zimativuta

    Kukhala na cikhulupililo.

    (KOLASI)

    O Yehova, ise tikupemphani

    Kuti mumvele pemphelo lathu.

    M’tiwonjezele cikhulupililo,

    Kuti’se tikulemekezeni.

  2. 2. Ngati tilibe cikhulupililo

    N’covuta kukukondweletsani.

    Koma ngati timakhulupilila,

    Tidzatumikila mosaopa.

    (KOLASI)

    O Yehova, ise tikupemphani

    Kuti mumvele pemphelo lathu.

    M’tiwonjezele cikhulupililo,

    Kuti’se tikulemekezeni.

(Onaninso Gen. 8:21; Aheb. 11:6; 12:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani