LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 80
  • ‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Talawani Ndipo Muone Kuti Yehova Ndi Wabwino”
    Imbirani Yehova
  • Nchito Yoonetsa Cikondi Cathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 80

NYIMBO 80

‘Talaŵani, Muone Kuti Yehova ni Wabwino’

Yopulinta

(Salimo 34:8)

  1. 1. Tikonda kutumikila

    Yehova Atate wathu.

    Tidzipeleka na mtima wonse

    Kuti’fe tilalikile.

    (KOLASI)

    Mau a M’lungu aitana:

    ‘Talaŵani muone.

    Kuti Yehova ni wabwino.’

    Mudzadalitsidwadi.

  2. 2. Mtumiki wanthawi zonse

    Amapeza madalitso.

    Pa zofunika za moyo wake

    Amadalila Yehova.

    (KOLASI)

    Mau a M’lungu aitana:

    ‘Talaŵani muone.

    Kuti Yehova ni wabwino.’

    Mudzadalitsidwadi.

(Onaninso Maliko 14:8; Luka 21:2; 1 Tim. 1:12; 6:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani