LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsa. 6
  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Limba Mtima, Ugwile Nchito Mwamphamvu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Kukhala Wolimba Mtima Sikovuta
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Kulitsani Makhalidwe Aumulungu—Kulimba Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nilimbitseni Mtima
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 October tsa. 6
Yesu akamba na atumwi ake okhulupilika

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 15-17

“Simuli Mbali ya Dzikoli”

15:19, 21; 16:33

  • Yesu anagonjetsa dziko mwa kusatengela nzelu za dziko ngakhale pang’ono

  • Otsatila a Yesu afunika kukhala olimba mtima kuti asadetsedwe na makhalidwe kapena zocita za anthu owazungulila

  • Kusinkha-sinkha citsanzo ca Yesu, amene anagonjetsa dziko, kungatithandize kukhala olimba mtima potengela citsanzo cake

Ni zinthu ziti zimene zingayese cikhulupililo canga pa nkhani yokhala mbali ya dziko?

Ni zinthu ziti za pa intaneti, TV, kapena pa wailesi zimene zinganipangitse kukhala mbali ya dziko?

M’bale wacicepele sakutengako mbali m’zocitika za dziko; m’bale akukana nchito inayake; m’bale akulalikila anzake; mlongo na mwamuna wake akukamba na dokota
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani