LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 149
  • Nyimbo ya Cipambano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Nyimbo ya Cipambano
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tiimbire Yehova Chifukwa Wapambana
    Imbirani Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • “Lalikila Mau”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 149

NYIMBO 149

Nyimbo ya Cipambano

Yopulinta

(Ekisodo 15:1)

  1. 1. Muimbileni Yehova M’lungu wokwezeka.

    Aŵaponya m’nyanja Aigupto onyada.

    Mutamandeni palibe

    Wolingana naye.

    Dzina ni Yehova wapambana

    Pa nkhondo.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu wokwezeka

    Ndimwe mwekha ‘mene simusintha.

    Mudzayeletsadi dzina lanu

    Na kuwononga oipa.

  2. 2. Mitundu yonse, ikutsutsana na Yehova.

    Adzaiwononga ngakhale

    Ni yamphamvu.

    Posacedwapa otsutsa

    Adzawonongedwa.

    Onse adzadziŵa Yehova

    Ni wamphamvu.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu wokwezeka

    Ndimwe mwekha ‘mene simusintha.

    Mudzayeletsadi dzina lanu

    Na kuwononga oipa.

(Onaninso Sal. 2:2, 9; 92:8; Malaki 3:6; Chiv. 16:16.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani