LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 139
  • Yelekeza Uli M’dziko Latsopano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yelekeza Uli M’dziko Latsopano
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yerekezerani Kuti Muli M’dziko Latsopano
    Imbirani Yehova
  • Imbani Nafe Nyimbo ya Ufumu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 139

NYIMBO 139

Yelekeza Uli M’dziko Latsopano

Yopulinta

(Chivumbulutso 21:1-5)

  1. 1. Udzione, unione

    Tili tonse m’dziko latsopano.

    Ganizila za mtendele

    Umene udzakhala m’dziko.

    Anthu ali na cimwemwe

    Mu ulamulilo wa M’lungu.

    Dziko latsopano layandikila.

    Na mtima wonse

    tidzaimba mokondwa:

    (KOLASI)

    “Yehova M’lungu tiyamikila

    Pa zonse imwe mwaticitila.

    Mwacimwemwe ise tikuimbilani.

    Zitamando na ulemu zonse n’zanu.”

  2. 2. Mudzione, munione,

    Tili tonse m’dziko latsopano.

    Zinthu zonse ni zabwino

    Palibe zocititsa mantha.

    Ananena, zacitika;

    Monga mwa cifunilo cake.

    Akufa onse adzaŵaukitsa;

    Capamodzi

    tidzaimbila Yehova:

    (KOLASI)

    “Yehova M’lungu tiyamikila

    Pa zonse imwe mwaticitila.

    Mwacimwemwe ise tikuimbilani.

    Zitamando na ulemu zonse n’zanu.”

(Onaninso Sal. 37:10, 11; Yes. 65:17; Yoh. 5:28; 2 Pet. 3:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani