LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 136
  • Yehova “Akufupe Mokwanila”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova “Akufupe Mokwanila”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
  • Ana a Mulungu Adzaonekela
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ana a Mulungu Adzaonekela
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 136

NYIMBO 136

Yehova “Akufupe Mokwanila”

Yopulinta

(Rute 2:12)

  1. 1. Yehova ni wokhulupilikadi;

    Saiŵala anthu ake.

    Iye adziŵa kuti nthawi zina

    Iwo amavutikadi.

    Ngati mwasiya nyumba na mabwenzi

    Kuti mumutumikile.

    Adziŵa kutaikilidwa kwanu,

    Adzakudalitsanidi.

    (KOLASI)

    O Yehova akudalitseni

    Akupatseni mphoto yabwino.

    Iye ni wokhulupilika,

    Sadzakusiyani; mudalileni.

  2. 2. Nthawi zina nkhawa za moyo wathu

    Zimaticulukiladi.

    Koma Yehova amasamalila

    Zonse ise timasoŵa.

    Iye amamvela ukapemphela

    Cifukwa amakukonda.

    Mwa mau ake na abale onse,

    Iye adzakutonthoza.

    (KOLASI)

    O Yehova akudalitseni

    Akupatseni mphoto yabwino.

    Iye ni wokhulupilika,

    Sadzakusiyani; mudalileni.

(Onaninso Ower. 11:38-40; Yes. 41:10.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani