LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 36
  • Titeteze Mitima Yathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Titeteze Mitima Yathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tetezani Mtima Wanu
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 36

NYIMBO 36

Titeteze Mitima Yathu

Yopulinta

(Miyambo 4:23)

  1. 1. Titeteze mtima wathu,

    Tipewe ucimo.

    Yehova adziŵa zonse

    Za mu mtima mwathu.

    Nthawi zina mtima wathu

    Ungatinamize.

    Conco tiganize bwino,

    Timvele Yehova.

  2. 2. Tikonzekeletse mtima,

    Tifune Yehova.

    Tim’tamande, tim’yamike,

    Amatisamala.

    Malangizo a Yehova,

    Tidzawatsatila.

    Tifuna kum’kondweletsa,

    Tsiku lililonse.

  3. 3. Titeteze mtima wathu

    Ku zinthu zoipa.

    Mau a Yehova M’lungu

    Adzatithandiza.

    Yehova adzatikonda

    Ngati tiyesetsa.

    Yehova ni bwenzi lathu.

    Ise tim’lambile.

(Onaninso Sal. 34:1; Afil. 4:8; 1 Pet. 3:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani