LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 90
  • Tilimbikitsane Wina na Mnzake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tilimbikitsane Wina na Mnzake
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tizilimbikitsana
    Imbirani Yehova
  • “Pitilizani Kutonthozana ndi Kulimbikitsana”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Khalanibe M’cikondi ca Mulungu
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • “Tiyeni Tilimbikitsane, Ndipo Tiwonjezele Kucita Zimenezi”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 90

NYIMBO 90

Tilimbikitsane Wina na Mnzake

Yopulinta

(Aheberi 10:24, 25)

  1. 1. Pamene tilimbikitsana

    Kutumikila Yehova.

    Cikondi cathu cimakula;

    Timapezadi cimwemwe.

    Cikondi timaonetsana,

    Cimatilimbikitsadi.

    Mpingo ni pothaŵila pathu,

    Ni malo a citetezo.

  2. 2. Mwa mau athu acikondi

    Timatonthozadi ena.

    Ndipo timaŵalimbikitsa

    Kuti iwo asafo’ke.

    Kumatipatsadi cimwemwe

    Kuseŵenzela pamodzi.

    Conco tizilimbikitsana

    Ndipo tizithandizana.

  3. 3. Tsiku la Atate Yehova,

    Tidziŵa layandikadi.

    Tifunika tizisonkhana

    Kuti tikapulumuke.

    Tiyeni tizithandizana

    Kusunga umphumphu wathu.

    Monga banja logwilizana

    Tidzalimbikitsanadi.

(Onaninso Luka 22:32; Mac. 14: 21, 22; Agal. 6:2; 1 Ates. 5:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani