LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 157
  • Mtendele Wosatha Pamapeto Pake!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mtendele Wosatha Pamapeto Pake!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
    Imbirani Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 157

NYIMBO 157

Mtendele Wosatha Pamapeto Pake!

Yopulinta

(Salimo 29:11)

  1. 1. M’dziko lamavuto

    Anthu a M’lungu

    Akukhala pamtendele.

    Ndipo tidziŵa

    kuti mavutowa

    Adzathadi

    posacedwa.

    (KOLASI)

    Pamapeto pake

    tidzauona

    Mtendele wosatha.

    Pa dziko lapansi

    na kumwambako,

    Konse kudzakhala

    Mtendele.

  2. 2. M’dziko la tsopano

    anthu onse

    Adzakhaladi amodzi.

    Ulamulilo

    tidzauonewo

    Udzakhala wacikondi.

    (KOLASI)

    Pamapeto pake

    tidzauona

    Mtendele wosatha.

    Pa dziko lapansi

    na kumwambako,

    Konse kudzakhala

    Mtendele.

    (KOLASI)

    Pamapeto pake

    tidzauona

    Mtendele wosatha.

    Pa dziko lapansi

    na kumwambako,

    Konse kudzakhala.

    (KOLASI)

    Pamapeto pake

    tidzauona

    Mtendele wosatha.

    Pa dziko lapansi

    na kumwambako,

    Konse kudzakhala

    Mtendele,

    Mtendele!

(Onaninso Sal. 72:1-7; Yes. 2:4; Aro. 16:20)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani