Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 23:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 23:28-30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Choncho Balaki anatenga Balamu nʼkupita naye pamwamba pa phiri la Peori, limene linayangʼanizana ndi Yesimoni.*+ 29 Kenako Balamu anauza Balaki kuti: “Mumange maguwa ansembe 7 pamalo ano ndipo mundikonzere ngʼombe zamphongo 7 ndi nkhosa zamphongo 7.”+ 30 Choncho Balaki anachita zimene Balamu ananena ndipo anapereka nsembe ngʼombe yamphongo ndi nkhosa yamphongo paguwa lililonse.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani