-
Numeri 23:28-30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Choncho Balaki anatenga Balamu nʼkupita naye pamwamba pa phiri la Peori, limene linayangʼanizana ndi Yesimoni.*+ 29 Kenako Balamu anauza Balaki kuti: “Mumange maguwa ansembe 7 pamalo ano ndipo mundikonzere ngʼombe zamphongo 7 ndi nkhosa zamphongo 7.”+ 30 Choncho Balaki anachita zimene Balamu ananena ndipo anapereka nsembe ngʼombe yamphongo ndi nkhosa yamphongo paguwa lililonse.
-