Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb19.09
  • Kuganizira Zoipa N’koopsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuganizira Zoipa N’koopsa
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • “Khalani Oyera”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo Padziko Lapansi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Musalole Kuti Zilakolako Zoipa Zizikulamulirani
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • “Sandulikani mwa Kusintha Maganizo Anu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19.09
M’bale akuganizira mayesero osiyanasiyana monga ndalama, galimoto yodula, fodya komanso mkazi yemwe akumukopa

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YAKOBO 1-2

Kuganizira Zoipa N’koopsa

1:14, 15

Maganizo oipa akakubwererani, muzichita zinthu zotsatirazi:

  • Muziwachotsa msanga n’kuyamba kuganizira zinthu zina.​—Afil. 4:8

  • Muziganizira mavuto amene angabwere ngati mutachita zoipazo.​—Deut. 32:29

  • Muzipemphera.​—Mat. 26:41

Maganizo oipa akandibwerera, kodi ndi zinthu zolimbikitsa ziti zomwe ndingayambe kuganizira?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani