Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb19.10 3
  • “Khalani Oyera”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Khalani Oyera”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Analenga Zamoyo Padziko Lapansi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • ‘Muzikumbukira Kukhalapo kwa Tsiku la Yehova’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Yehova Amafuna Kuti Anthu Ake Akhale Oyera
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • Tingatani Kuti Mulungu Azitiona Kuti Ndife Oyera?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19.10 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 PETULO 1-2

“Khalani Oyera”

1:14-16

Tiyenera kukhala oyera, kapena kuti aukhondo kuti Yehova azisangalala ndi kulambira kwathu. Kodi timakhala bwanji oyera . . .

  • M’bale wachinyamata wakonzeka kuti azipita kumisonkhano koma bambo ake omwe si Amboni akumukalipira

    mwauzimu?

  • Mwamuna ndi mkazi wake akufufuza pagulu la mafilimu achiwerewere, oonetsa zachiwawa komanso azamatsenga kuti apeze filimu yomwe angaonere

    mwamakhalidwe?

  • Mzimayi akutsuka poto

    mwakuthupi

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani