Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb20.07 11
  • July 27–August 2, 2020

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 27–August 2, 2020
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20.07 11

July 27–August 2

EKISODO 12

  • Nyimbo Na. 20 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kufunika kwa Mwambo wa Pasika kwa Akhristu”: (10 min.)

    • Eks 12:5-7​—Kufunika kwa mwana wa nkhosa wa pa Pasika (w07 1/1 20 ¶4)

    • Eks 12:12, 13​—Kufunika kwa magazi omwe anapakidwa pamafelemu a zitseko (it-2 583 ¶6)

    • Eks 12:24-27​—Zimene tingaphunzire kuchokera pa zomwe zinkachitika pa mwambo wa Pasika (w13 12/15 20 ¶13-14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 12:12​—N’chifukwa chiyani miliri imene inagwera Aiguputo, makamaka wa 10, kunali kuweruza milungu yawo yonyenga? (it-2 582 ¶2)

    • Eks 12:14-16​—Mofanana ndi misonkhano ina yopatulika, kodi Chikondwerero cha Mikate Yopanda Chofufumitsa chinali chapadera m’njira iti, nanga chinkathandiza bwanji Aisiraeli? (it-1 504 ¶1)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 12:1-10 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 2)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako mugawireni magazini yaposachedwapa yomwe ili ndi nkhani yomwe mwakambirana. (th phunziro 6)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) bhs 16 ¶21-22 (th phunziro 19)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 38

  • “Yehova Amateteza Anthu Ake”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Kuona Malo Osungirako Zinthu Zakale ku Warwick: “Anthu Odziwika ndi Dzina la Yehova”.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia 6:9-18

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 41 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani