Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.01 18
  • February 14-20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 14-20
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.01 18

February 14-20

1 SAMUELI 3-5

  • Nyimbo Na. 1 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Amatiganizira”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • 1Sa 3:3​—Kodi tikudziwa bwanji kuti Samueli sanagone m’Malo Oyera Koposa? (w05 3/15 21 ¶6)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Sa 3:1-18 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. M’pempheni kuti muziphunzira naye Baibulo pogwiritsa ntchito kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale. (th phunziro 11)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. M’patseni kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, ndipo yambitsani phunziro la Baibulo pa phunziro 01. (th phunziro 15)

  • Phunziro la Baibulo: (5 min.) lffi phunziro 03 mfundo 6 (th phunziro 14)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 30

  • “Zimene Tingaphunzire kwa Samueli”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Zimene Tingaphunzire Kuchokera kwa Samueli.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 11:10-17

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani