Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.01 19
  • Yehova Amatiganizira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amatiganizira
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Tizidzichepetsa Zinthu Zikatiyendera
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Zimene Tingaphunzire kwa Samueli
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • “Ndinamutsutsa Pamasom’pamaso”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Kumvera Kumaposa Nsembe
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.01 19
Zithunzi: 1. Samueli ali mwana akumvetsera pamene Yehova akumulankhula. 2. Samueli akuuza Eli uthenga wochokera kwa Yehova.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yehova Amatiganizira

Samueli ankaganiza kuti Eli akumuitana (1Sa 3:4-7; w18.09 4:3)

Yehova anatsimikizira Samueli kuti iyeyo ndi amene amamuitana (1Sa 3:8, 9)

Yehova anasonyeza kuti ankaganizira Samueli yemwe anali wamng’ono (1Sa 3:15-18; w18.09 4:4)

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimaganizira achinyamata komanso achikulire? Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimaganizira ena ndikakhala kumisonkhano ya Chikhristu?’

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani