Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • lfb sect. 12
  • Mawu Oyamba Gawo 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 12
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Oyamba Gawo 11
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Yehova Amamvetsera Mapemphero Athu?
    Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
  • Kodi Yesu Anachita Zotani Ali Padzikoli?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Tili Ndi Mwayi Wopemphera kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb sect. 12
Yesu akuphunzitsa akuluakulu ndi ana omwe

Mawu Oyamba Gawo 12

Yesu anaphunzitsa anthu zokhudza Ufumu wakumwamba. Iye anawaphunzitsanso kuti azipemphera kuti dzina la Mulungu liyeretsedwe, Ufumu wake ubwere komanso kuti zimene Mulungu amafuna zichitike padzikoli. Ngati ndinu kholo, fotokozerani mwana wanu chifukwa chake pempheroli ndi lofunika kwa ife. Yesu sanalole kuti Satana amulepheretse kukhala wokhulupirika kwa Mulungu. Iye anasankha atumwi ake ndipo iwo ndi amene anali oyamba kusankhidwa kuti adzalamulire nawo mu Ufumu. Thandizani mwana wanuyo kuti aone zoti Yesu anali wodzipereka kwambiri pa kulambira koona. Popeza Yesu ankafuna kuthandiza anthu anachiritsa odwala, anadyetsa anjala komanso anaukitsa akufa. Zinthu zodabwitsa zimene anachitazi zinasonyeza zimene Ufumu wa Mulungu udzachitire anthu.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Yesu anauza otsatira ake kuti azilalikira za Ufumu komanso azithandiza anthu kuti akhale ophunzira ake

  • Popemphera, tizinena kaye zinthu zokhudza Yehova tisanapemphe zokhudza ifeyo

  • Tizikhululuka ndi mtima wonse ndiponso tizichitira anthu zimene tingafune kuti iwowo atichitire

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani