Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.10 6
  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Simuli Mbali ya Dzikoli”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Limba Mtima Ndipo Ugwire Ntchitoyi’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kukhala Olimba Mtima Sikovuta Kwambiri
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • “Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.10 6
Yesu akulankhula ndi atumwi ake okhulupirika

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 15-17

“Simuli Mbali ya Dzikoli”

15:19, 21; 16:33

  • Yesu anagonjetsa dziko popewa kuchita zinthu za m’dzikoli

  • Otsatira a Yesu amayenera kuchita zinthu molimba mtima kuti asasokonezeke ndi maganizo komanso zochita za anthu a m’dzikoli

  • Kutengera chitsanzo cha Yesu yemwe anagonjetsa dziko kungatithandize kuti tizichita zinthu molimba mtima

Kodi ndi zinthu ziti zimene zingachititse kuti ndikhale mbali ya dzikoli?

Kodi ndi zinthu ziti zomwe zimafalitsidwa pa TV, m’manyuzipepala kapena pa intaneti zimene zingachititse kuti ndikhale mbali ya dzikoli?

M’bale wachichepere sakuimba nawo nyimbo yafuko; m’bale akukana ntchito inayake; m’bale akulalikira anzake; m’bale ndi mkazi wake akulankhulana ndi dokotala
    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani