Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.05 14
  • Yehova Anachita Pangano ndi Davide

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Anachita Pangano ndi Davide
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Muzidalira Yehova Kuti Akuthandizeni
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • ‘Madalitso Onsewa . . . Adzakupeza’
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Musamaone Zinthu Zopanda Pake
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.05 14
Mfumu Davide ili pawindo la nyumba yachifumu, ndipo ikuyang’ana panja.

Davide akuganizira mozama za pangano limene Yehova anapangana naye

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yehova Anachita Pangano ndi Davide

Yehova analonjeza Davide kuti adzakhazikitsa ufumu m’banja lake (2Sa 7:11, 12; w10 4/1 20 ¶3; onani chithunzi chapachikuto)

Mbali zina za pangano limene Yehova anachita ndi Davide zinakwaniritsidwa pa Mesiya (2Sa 7:13, 14; w10 4/1 20 ¶4)

Zinthu zabwino zimene zinabwera chifukwa cha ulamuliro wa Mesiya zidzakhalapo mpaka kalekale (2Sa 7:15, 16; Ahe 1:8; w14 10/15 10 ¶14)

Yesu ali kumwamba pampando wachifumu ndipo akuyang’ana dziko lapansi.

Dzuwa ndi mwezi zimatikumbutsa kuti ulamuliro wa Mesiya udzakhalapo mpaka kalekale. (Sl 89:35-37) Mukamaona zinthu zimenezi muziganizira madalitso amene Yehova anakulonjezani inuyo komanso anthu a m’banja lanu kudzera mu Ufumu wake.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani