Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb22.05 25
  • Abisalomu Anaukira Chifukwa cha Kunyada

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abisalomu Anaukira Chifukwa cha Kunyada
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Kudzikonda kwa Aminoni Kunabweretsa Mavuto
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Kodi Mumapereka Nsembe?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yehova ndi Mulungu Wachilungamo
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22.05 25
Abisalomu wagwada patsogolo pa atumiki ake komanso Aisiraeli ena ndipo akuyankhula ndi bambo amene akumuweramira.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Abisalomu Anaukira Chifukwa cha Kunyada

Abisalomu anadzifunira yekha ulemerero (2Sa 15:1; it-1 860)

Abisalomu anakopa mitima ya anthu (2Sa 15:2-6; w12 7/15 13 ¶5)

Abisalomu ankafuna kulanda ufumu wa bambo ake (2Sa 15:10-12; it-1 1083-1084)

Tisalole kuti kulakalaka kwambiri zinthu kuzilamulira mtima wathu. Koma nthawi ndi nthawi tizionanso zimene timalakalaka. M’malo momangofuna kugometsa anthu ena, tiziyesetsa kuganiziranso zofuna zawo.​—Afi 2:3, 4.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani