Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb23.11 3
  • ‘Muziika Kenakake Pambali’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Muziika Kenakake Pambali’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • “Khalani Opatsa”
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Timathokoza Yehova Chifukwa cha Chikondi Chanu
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • ‘Timakobidi Tiwiri Tating’ono’ Tamtengo Wapatali
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • “Muzipereka Mphatso kwa Yehova”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23.11 3
Mlongo wachikulire akuponya ndalama m’bokosi la zopereka m’Nyumba ya Ufumu. Zithunzi: 1. Abale ndi alongo akugwira ntchito yazomangamanga. 2. Pulogalamu ya JW Broadcasting®. 3. Abale ndi alongo akutsitsa mugalimoto katundu wothandizira anthu pa ngozi zadzidzidzi.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

‘Muziika Kenakake Pambali’

Tisamapereke ndalama zothandizira pa ntchito za Ufumu mongodzidzimukira. M’malomwake, tizichita monga mmene Mtumwi Paulo anatilimbikitsira kuti, nthawi zonse ‘tiziika kenakake pambali.’ (1Ak 16:2) Tikamatsatira malangizo ouziridwawa, timakhala tikuthandiza pa kulambira koyera komanso timasangalala. Kaya zopereka zathu zikhale zochepa bwanji, Yehova amatiyamikira kwambiri chifukwa chofunitsitsa kumulemekeza ndi zinthu zathu zamtengo wapatali.—Miy 3:9.

ONERANI VIDIYO YAKUTI TIKUKUTHOKOZANI CHIFUKWA MUMAIKA KENAKAKE PAMBALI, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi kupangiratu pulani ya ndalama zoti tikapereke n’kothandiza bwanji?

  • Kodi ena anachita zotani kuti ‘aziika kenakake pambali’?

DZIWANI ZAMBIRI PAWEBUSAITI YATHU

Chizindikiro cha “Donations” chosonyeza dzanja litanyamula ndalama ya chitsulo.

Kodi mungapereke bwanji ndalama zothandizira ntchito ya Mboni za Yehova? Dinani pamene alemba kuti “Donations” m’munsi mwa tsamba loyamba la JW Library®. M’mayiko ambiri, pangakhale linki ina yopita ku nkhani yonena za Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri ya mutu wakuti Zopereka Zopita ku Gulu la Mboni za Yehova—Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani