Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.04 4
  • “Machimo Ako Akhululukidwa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Machimo Ako Akhululukidwa”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Chozizwitsa Choyamba cha Yesu
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • “Khalani Oyera”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo Padziko Lapansi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.04 4
Yesu ali pampando wake wachifumu kumwamba

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIKO 1-2

“Machimo Ako Akhululukidwa”

2:5-12

Akulowetsa munthu wakufa ziwalo kudzera padenga kuti afike kwa Yesu

Kodi tikuphunzirapo chiyani pa chozizwitsa chimenechi?

  • Timadwala chifukwa chakuti tinatengera uchimo

  • Yesu ali ndi mphamvu zokhululukira machimo komanso kuchiritsa odwala

  • Mu Ufumu wa Mulungu, Yesu adzathetsa uchimo komanso matenda

Kodi lemba la Maliko 2:5-12 lingandithandize bwanji kupirira ndikamadwala?

Munthu wosaona akuona, wolumala wachoka panjinga yake akuyenda
    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani