Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Bambo ake anapitiriza ulendo wopita kwawo kwa mkazi uja, ndipo Samisoni anakonza phwando kumeneko,+ popeza umu ndi mmene achinyamata anali kuchitira.

  • Mateyu 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Ufumu wakumwamba uli ngati mfumu imene inakonza phwando la ukwati+ wa mwana wake.

  • Chivumbulutso 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mngeloyo anandiuza kuti: “Lemba: Odala ndiwo amene aitanidwa+ ku phwando la chakudya chamadzulo la ukwati+ wa Mwanawankhosa.” Anandiuzanso kuti: “Awa ndi mawu oona a Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena