53 Atiweruze mulungu wa Abulahamu,+ mulungu wa Nahori,+ yemwe ali mulungu wa bambo awo.” Koma Yakobo analumbira pa Mulungu amene bambo ake Isaki anali kumuopa.+
13 Yehova wa makamu ndi amene muyenera kumuona kuti ndi woyera,+ ndipo iyeyo ndi amene muyenera kumuopa.+ Iye ndi amene ayenera kukuchititsani kunjenjemera.”+