Salimo 2:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Tumikirani Yehova mwamantha.+Kondwerani ndipo nthunthumirani.+ Salimo 76:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Inu ndinu wochititsa mantha,+Ndani angaime pamaso panu inu mutakwiya kwambiri?+ Yesaya 66:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 “Zinthu zonsezi ndinazipanga ndi dzanja langa, choncho zinakhalapo,”+ akutero Yehova. “Ine ndidzayang’ana munthu amene ali wosautsidwa, wosweka mtima,+ ndiponso wonjenjemera ndi mawu anga.+ Malaki 2:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 “Pangano limene ndinapangana naye linasunga moyo wake. Linamuthandizanso kukhala ndi moyo wamtendere.+ Chifukwa cha madalitso amenewa, anali kundiopa.+ Popeza kuti anali kulemekeza dzina langa, sankachita chilichonse chondikwiyitsa.+ Afilipi 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Chotero, okondedwa anga, monga mmene mwakhalira omvera nthawi zonse,+ osati pokhapokha ine ndikakhalapo,* koma mofunitsitsa kwambiri tsopano pamene ine kulibe, pitirizani kukonza chipulumutso chanu, mwamantha+ ndi kunjenjemera.
2 “Zinthu zonsezi ndinazipanga ndi dzanja langa, choncho zinakhalapo,”+ akutero Yehova. “Ine ndidzayang’ana munthu amene ali wosautsidwa, wosweka mtima,+ ndiponso wonjenjemera ndi mawu anga.+
5 “Pangano limene ndinapangana naye linasunga moyo wake. Linamuthandizanso kukhala ndi moyo wamtendere.+ Chifukwa cha madalitso amenewa, anali kundiopa.+ Popeza kuti anali kulemekeza dzina langa, sankachita chilichonse chondikwiyitsa.+
12 Chotero, okondedwa anga, monga mmene mwakhalira omvera nthawi zonse,+ osati pokhapokha ine ndikakhalapo,* koma mofunitsitsa kwambiri tsopano pamene ine kulibe, pitirizani kukonza chipulumutso chanu, mwamantha+ ndi kunjenjemera.