Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo anayamba kusonkhana kwa ine, aliyense akunjenjemera+ chifukwa cha mawu a Mulungu wa Isiraeli otsutsa kusakhulupirika kwa anthu amene anabwerera kuchokera ku ukapolo. Pa nthawiyi n’kuti ine nditakhala pansi ndili wokhumudwa ndi wachisoni kwambiri, ndipo ndinakhala choncho mpaka nthawi yopereka nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Salimo 119:161
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 161 Akalonga andizunza popanda chifukwa,+

      Koma mtima wanga umaopa mawu anu.+

  • Machitidwe 16:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Pamenepo anapempha kuti amupatse nyale ndipo analumphira mkatimo. Akunjenjemera ndi mantha, anagwada+ pamaso pa Paulo ndi Sila.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena