Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Aliyense amene anaopa mawu a Yehova pakati pa atumiki a Farao anaonetsetsa kuti ziweto zake ndi antchito ake athawira m’nyumba.+

  • 2 Mafumu 22:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 chifukwa chakuti mtima wako+ unali wofewa ndipo unadzichepetsa+ chifukwa cha Yehova utamva zimene ndanena zotsutsana ndi malo ano ndi anthu ake, kuti malowa adzakhala chodabwitsa ndi temberero,+ unang’amba+ zovala zako n’kuyamba kulira pamaso panga, ineyo ndamva,” ndiwo mawu a Yehova.+

  • Yesaya 66:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Zinthu zonsezi ndinazipanga ndi dzanja langa, choncho zinakhalapo,”+ akutero Yehova. “Ine ndidzayang’ana munthu amene ali wosautsidwa, wosweka mtima,+ ndiponso wonjenjemera ndi mawu anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena