Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno Esau anapempha Yakobo kuti: “Chonde, fulumira ndipatseko chakudya chofiiracho pang’ono, icho chofiiracho! Ndatopatu ine!” Ndiye chifukwa chake anatchedwa Edomu.*+

  • Oweruza 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova, pamene munayenda kuchokera ku Seiri,+

      Pamene munaguba kuchokera kudera la Edomu,+

      Dziko linagwedezeka,+ kumwamba kunagwetsa madzi,+

      Mitambo inagwetsa madzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena