Genesis 6:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndiyeno ana a Mulungu+ woona anayamba kuona+ kuti ana aakazi a anthu anali okongola. Chotero, anayamba kudzitengera okha akazi alionse amene anawasankha. Genesis 34:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Anaphanso Hamori ndi mwana wake Sekemu ndi lupanga.+ Kenako anatenga Dina m’nyumba ya Sekemu, n’kupita naye.+ Deuteronomo 22:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 mwamunayo azipereka masekeli 50 asiliva kwa bambo a mtsikanayo,+ ndipo akhale mkazi wake chifukwa chakuti wamunyazitsa. Sadzaloledwa kumusiya ukwati masiku onse a moyo wake.+ 2 Samueli 13:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Koma Aminoni sanamvere mawu ake. Popeza anali ndi mphamvu zoposa Tamara, anamuchititsa manyazi+ mwa kugona naye.+ 1 Akorinto 6:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Thawani dama.+ Tchimo lililonse limene munthu angachite ndi la kunja kwa thupi lake, koma amene amachita dama amachimwira thupi lake.+
2 Ndiyeno ana a Mulungu+ woona anayamba kuona+ kuti ana aakazi a anthu anali okongola. Chotero, anayamba kudzitengera okha akazi alionse amene anawasankha.
26 Anaphanso Hamori ndi mwana wake Sekemu ndi lupanga.+ Kenako anatenga Dina m’nyumba ya Sekemu, n’kupita naye.+
29 mwamunayo azipereka masekeli 50 asiliva kwa bambo a mtsikanayo,+ ndipo akhale mkazi wake chifukwa chakuti wamunyazitsa. Sadzaloledwa kumusiya ukwati masiku onse a moyo wake.+
14 Koma Aminoni sanamvere mawu ake. Popeza anali ndi mphamvu zoposa Tamara, anamuchititsa manyazi+ mwa kugona naye.+
18 Thawani dama.+ Tchimo lililonse limene munthu angachite ndi la kunja kwa thupi lake, koma amene amachita dama amachimwira thupi lake.+