Deuteronomo 28:65 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 65 Pakati pa mitundu imeneyo sudzakhala mwamtendere,+ ndipo sudzapeza malo oti phazi lako liponde kuti lipumulirepo. Kumeneko, Yehova adzakupatsa mtima wachinthenthe,+ adzachititsa maso ako+ khungu ndipo adzakutayitsa mtima. Miyambo 28:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Munthu wolemedwa ndi mlandu wokhetsa magazi a munthu adzakhala wothawathawa mpaka kumanda.+ Anthu asamugwire n’cholinga choti amuletse. Hoseya 9:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Mulungu wanga+ adzawakana chifukwa sanamumvere,+ ndipo iwo adzakhala othawa kwawo pakati pa mitundu ina.+
65 Pakati pa mitundu imeneyo sudzakhala mwamtendere,+ ndipo sudzapeza malo oti phazi lako liponde kuti lipumulirepo. Kumeneko, Yehova adzakupatsa mtima wachinthenthe,+ adzachititsa maso ako+ khungu ndipo adzakutayitsa mtima.
17 Munthu wolemedwa ndi mlandu wokhetsa magazi a munthu adzakhala wothawathawa mpaka kumanda.+ Anthu asamugwire n’cholinga choti amuletse.
17 Mulungu wanga+ adzawakana chifukwa sanamumvere,+ ndipo iwo adzakhala othawa kwawo pakati pa mitundu ina.+