Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma ine chikhulupiriro changa chili mwa inu Yehova.+

      Ndipo ndikunena kuti: “Inu ndinu Mulungu wanga.”+

  • Yesaya 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chotero mneneriyo anati: “Tamverani inu a nyumba ya Davide. Kodi mukuona ngati n’zazing’ono kuti muzitopetsa anthu, ndiponso kuti mutopetse Mulungu wanga?+

  • Mika 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma ine ndidzadikirira Yehova.+ Ndidzayembekezera moleza mtima Mulungu wa chipulumutso changa.+ Mulungu wanga adzandimvera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena