Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithu ndidzayembekezera chipulumutso kwa inu, Yehova.+

  • Salimo 25:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndiyendetseni m’choonadi chanu ndi kundiphunzitsa,+

      Pakuti inu ndinu Mulungu wa chipulumutso changa.+

      ו [Waw]

      Chiyembekezo changa chili mwa inu tsiku lonse.+

  • Salimo 62:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndithudi, moyo wanga ukuyembekezera Mulungu modekha.+

      Chipulumutso changa chidzachokera kwa iye.+

  • Maliro 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndi bwino kuti munthu ayembekezere+ chipulumutso cha Yehova+ moleza mtima.+

  • Luka 2:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiyeno mu Yerusalemu munali munthu wina dzina lake Simiyoni. Mwamuna ameneyu anali wolungama ndi woopa Mulungu. Anali kuyembekezera nthawi imene Mulungu adzatonthoze Isiraeli,+ ndipo mzimu woyera unali pa iye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena