Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Paja kale makolo athu anapita ku Iguputo,+ ndipo tinakhala kumeneko zaka zambiri.+ Aiguputowo anatizunza ife ndi makolo athu.+

  • Salimo 105:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kenako Isiraeli anapita ku Iguputo,+

      Yakobo anakhala monga mlendo m’dziko la Hamu.+

  • Yesaya 52:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pakuti Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Poyamba anthu anga anapita ku Iguputo kuti akakhale ngati alendo.+ Ndiyeno Asuri anawapondereza popanda chifukwa.”

  • Machitidwe 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yakobo anapita ku Iguputo+ kumene iye ndi makolo athu+ aja anamwalirira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena