Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamene Abulamu anali ndi zaka 99, Yehova anaonekera kwa iye n’kumuuza kuti:+ “Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse.+ Yenda pamaso panga ndipo ukhale wolungama.+

  • Genesis 24:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Iye anandiyankha kuti, ‘Yehova, amene ndakhala ndikuyenda pamaso pake movomerezeka,+ atumiza mngelo+ wake kuti apite nawe limodzi, ndipo ameneyo akakuthandiza ndithu kuti ukapeze chimene uyendere.+ Kumeneko, ukam’tengere mkazi mwana wanga, kwa abale anga, kubanja la bambo anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena