-
Genesis 48:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Pamenepo anadalitsa Yosefe,+ kuti:
“Mulungu woona amene makolo anga Abulahamu ndi Isaki anayenda pamaso pake,+
Mulungu woona amene wakhala m’busa wanga moyo wanga wonse mpaka lero,+
-