Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova amandipatsa mphoto mogwirizana ndi chilungamo changa.+

      Amandibwezera mogwirizana ndi kuyera kwa manja anga.+

  • Yohane 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Wolankhula za m’maganizo mwake amadzifunira yekha ulemerero.+ Koma wofunira ulemerero iye amene anamutuma, ameneyu ali woona, ndipo mwa iye mulibe kusalungama.

  • Aroma 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pajatu Mose analemba kuti munthu wochita chilungamo cha m’Chilamulo adzakhala ndi moyo chifukwa cha chilungamo chimenecho.+

  • 1 Yohane 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Aliyense amene ali mwana wa Mulungu sapitiriza kuchita tchimo,+ chifukwa mbewu ya Mulungu yopatsa moyo imakhalabe mwa munthu ameneyo, ndipo sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo, chifukwa ndi mwana wa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena