18 Wolankhula za m’maganizo mwake amadzifunira yekha ulemerero.+ Koma wofunira ulemerero iye amene anamutuma, ameneyu ali woona, ndipo mwa iye mulibe kusalungama.
9 Aliyense amene ali mwana wa Mulungu sapitiriza kuchita tchimo,+ chifukwa mbewu ya Mulungu yopatsa moyo imakhalabe mwa munthu ameneyo, ndipo sakhala ndi chizolowezi chochita tchimo, chifukwa ndi mwana wa Mulungu.+