Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Udzalowe nazo ziwiriziwiri za mtundu uliwonse. Zolengedwa zouluka monga mwa mitundu yawo, nyama zoweta monga mwa mitundu yawo,+ nyama zonse zokwawa panthaka monga mwa mitundu yawo, kuti zidzasungike zamoyo.+

  • Levitiko 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 ndi mtundu uliwonse wa khwangwala.+

  • 1 Mafumu 17:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Uzikamwa+ madzi mumtsinje umene uli m’chigwacho, ndipo ndidzalamula akhwangwala+ kuti azikakupatsa chakudya.”+

  • Yobu 38:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndani amakonzera khwangwala chakudya,+

      Ana ake akamalirira Mulungu kuti awathandize,

      Akamadzandira chifukwa chosowa chakudya?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena